fbpx

Ndife bungwe la chitukuko lomwe likulu lake lili ku Switzerland ndi ofesi ina ku Malawi. Pakadali pano tikugwira ntchito zathu ku Malawi ndipo tikufunitsitsa kuti anthu okwana 100’000 afikiridwa, ndipo kuti pofika 2020 anthu afikilidwa m’madera atatu awa:

Icon_Bildung

Maphunziro

Mwana aliyense ali ndi ufulu wa maphunziro
Kudzera ku ma phunziro kuthekera kwanu konse kumatulukira.

Phunzirani zambiri

Icon_Gesundheit

Zaumoyo

Tikulimbikitsa umoyo wabwino ndi wathanzi kwa ana

Phunzirani zambiri

Icon_Arbeitsplatze

Ntchito

Timakhulupilira kuthekera kwa munthu
Timalenga ntchito zomwe tikupereka mwayi ochuluka kwa anthu

Phunzirani zambiri

«Kuyambira chaka cha 2012 takhala tikugwira ntchito ndikuonetsetsa kuti ana 100’000 aku Malawi ali ndi mwayi wa maphunziro, moyo wathanzi, ndi zamasewero. Ana a ku Malawi akhale ndi chiyembekezo ndikutenga tsogolo lawo m’manja mwao.»

– Simon Holdener, Oyambitsa bungwe